2 Samueli 19:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo Barizilai anali nkhalamba, ndiye wa zaka makumi asanu ndi atatu; ndiye amene anapereka chakudya kwa mfumu muja anagona ku Mahanaimu, pakuti anali munthu womveka ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo Barizilai anali nkhalamba, ndiye wa zaka makumi asanu ndi atatu; ndiye amene anapereka chakudya kwa mfumu muja anagona ku Mahanaimu, pakuti anali munthu womveka ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Barizilai anali munthu wokalamba, wa zaka 80 zakubadwa. Ndipo iye ndiye ankapatsa mfumu chakudya nthaŵi imene mfumuyo inkakhala ku Mahanaimu, pakuti iyeyo anali munthu wolemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Tsono Barizilai anali wokalamba kwambiri, wa zaka makumi asanu ndi atatu. Iye ndi amene anapereka zinthu kwa mfumu pamene anali ku Mahanaimu pakuti anali wolemera kwambiri. Onani mutuwo |