Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 18:25 - Buku Lopatulika

25 Pamenepo mlondayo anafuula, nauza mfumu. Mfumuyo niti, Ngati ali yekha alikubwera ndi mau. Ndipo iye uja anayenda msanga, nayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Pamenepo mlondayo anafuula, nauza mfumu. Mfumuyo niti, Ngati ali yekha alikubwera ndi mau. Ndipo iye uja anayenda msanga, nayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Ndipo mlondayo adafuula nauza mfumu. Mfumuyo idati, “Ngati ali yekhayekha, ndiye kuti ali ndi nkhani yabwino.” Tsono munthu uja adafika ndithu, nayandikira pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Mlonda uja anapita kwa mfumu ndipo anafotokoza. Mfumu inati, “Ngati ali yekha ali ndi nkhani yabwino” Ndipo munthuyo anayandikira.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 18:25
3 Mawu Ofanana  

Koma Davide anakhala pakati pa zipata ziwiri; ndipo mlonda anakwera pa tsindwi la chipata cha kulinga, natukula maso ake, napenya; naona munthu alikuthamanga yekha.


Ndipo mlondayo anaona munthu wina wothamanga; mlonda naitana wakuchipata nanena, Taona munthu wina wakuthamanga yekha. Ndipo mfumu inati, Iyenso abwera ndi mau.


Pakuti Ambuye atero kwa ine, Muka, ika mlonda anene chimene achiona;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa