Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 17:5 - Buku Lopatulika

5 Pomwepo Abisalomu anati, Kaitane tsopano Husai Mwariki yemwe, timvenso chimene anene iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pomwepo Abisalomu anati, Kaitane tsopano Husai Mwariki yemwe, timvenso chimene anene iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Apo Abisalomu adati, “Muitanenso Husai, Mwariki, ndipo timvenso zimene anene.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Koma Abisalomu anati, “Muyitanenso Husai Mwariki kuti timve zimene iye adzanena.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo wina anauza Davide nati, Ahitofele ali pakati pa opangana chiwembu pamodzi ndi Abisalomu. Davide nati, Yehova, musandulize uphungu wa Ahitofele ukhale wopusa.


Ndipo mauwa anamuyenerera Abisalomu, ndi akulu onse a Israele.


Ndipo pakufika Husai kwa Abisalomu, Abisalomuyo ananena naye, Ahitofele analankhula mau akuti; tichite kodi monga mwa kunena kwake? Ngati iai, unene ndiwe.


nati kwa iwo, Kodi inu mundipangire bwanji kuti tiyankhe anthu awa anandiuza ine, kuti, Mupepuze goli limene atate wanu anatisenza ife?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa