Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 17:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Koma Abisalomu anati, “Muyitanenso Husai Mwariki kuti timve zimene iye adzanena.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Pomwepo Abisalomu anati, Kaitane tsopano Husai Mwariki yemwe, timvenso chimene anene iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pomwepo Abisalomu anati, Kaitane tsopano Husai Mwariki yemwe, timvenso chimene anene iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Apo Abisalomu adati, “Muitanenso Husai, Mwariki, ndipo timvenso zimene anene.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:5
6 Mawu Ofanana  

Tsono Davide anamva kuti, “Ahitofele ali pakati pa anthu owukira pamodzi ndi Abisalomu.” Choncho Davide anapemphera, “Inu Yehova, musandutse uphungu wa Ahitofele ukhale uchitsiru.”


Malangizo awa anaoneka abwino kwa Abisalomu ndi kwa akuluakulu onse a Israeli.


Husai atabwera kwa iye, Abisalomu anati, “Ahitofele wapereka malangizo ake. Kodi tichite zimene wanena? Ngati sichoncho, tiwuze maganizo ako.”


Iye anawafunsa kuti, “Kodi malangizo anu ngotani? Kodi ndiwayankhe chiyani anthu amene akunena kwa ine kuti, ‘Peputsani goli limene abambo anu anatisenzetsa’?”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa