Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 17:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo kunali, atapita iwo, ajawo anatuluka m'chitsime, nanka nauza mfumu Davide; nati kwa Davide, Nyamukani nimuoloke madzi msanga; pakuti Ahitofele anapangira zotere pa inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo kunali, atapita iwo, ajawo anatuluka m'chitsime, namka nauza mfumu Davide; nati kwa Davide, Nyamukani nimuoloke madzi msanga; pakuti Ahitofele anapangira zotere pa inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Ankhondo aja atapita, anthuwo adatuluka m'chitsime muja, ndipo adakauza mfumu Davide kuti, “Nyamukani, muwoloke mtsinje mofulumira, popeza kuti Ahitofele walangiza anthu ake zokuthirani nkhondo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Anthu aja atapita, awiriwo anatuluka mʼchitsimemo ndipo anapita kukawuza mfumu Davide nati kwa iye, “Nyamukani, muwoloke mtsinje msangamsanga. Ahitofele wapereka malangizo akutiakuti kutsutsana nanu.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:21
3 Mawu Ofanana  

Pomwepo Davide ananyamuka ndi anthu onse amene anali naye, naoloka Yordani. Kutacha m'mawa sanasowe mmodzi wa iwo wosaoloka Yordani.


Onani, ndikadathawira kutali, ndikadagona m'chipululu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa