Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 17:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo mkazi anatenga chivundikiro nachiika pakamwa pa chitsime, napapasapo lipande la tirigu; momwemo sichinadziwike.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo mkazi anatenga chivundikiro nachiika pakamwa pa chitsime, napapasapo lipande la tirigu; momwemo sichinadziwika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Tsono mkazi wa munthu uja adatenga chivundikiro, nachiika pamwamba pa chitsimecho, nkuyanikapo tirigu, kotero kuti chitsimecho sichinkadziŵika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mkazi wake anatenga chophimba ndipo anachiyika pamwamba pa chitsimecho nawazapo tirigu. Palibe amene anadziwa chilichonse za izi.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:19
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anamwino ananena ndi Farao, Popeza akazi a Ahebri safanana ndi akazi a Aejipito; pakuti ali ndi mphamvu, naona ana asanafike anamwino.


Ndipo Mose anatuluka kwa Farao m'mzinda nakweza manja ake kwa Yehova; ndipo mabingu ndi matalala analeka, ndi mvula siinavumbanso padziko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa