2 Samueli 16:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo kunali pakudza kwa Abisalomu Husai Mwariki, bwenzi la Davide, Husai ananena ndi Abisalomu, Mfumu ikhale ndi moyo. Mfumu ikhale ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo kunali pakudza kwa Abisalomu Husai Mwariki, bwenzi la Davide, Husai ananena ndi Abisalomu, Mfumu ikhale ndi moyo. Mfumu ikhale ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndipo pamene Husai Mwariki, bwenzi la Davide, adakumana ndi Abisalomu, adafuula kwa Abisalomuyo kuti, “Amfumu akhale ndi moyo wautali! Amfumu akhale ndi moyo wautali!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono Husai Mwariki bwenzi la Davide anapita kwa Abisalomu ndipo anati kwa iye, “Ikhale ndi moyo wautali mfumu! Ikhale ndi moyo wautali mfumu!” Onani mutuwo |