2 Samueli 15:21 - Buku Lopatulika21 Itai nayankha mfumu nuti, Pali Yehova, pali mbuye wanga mfumu, zoonadi apo padzakhala mbuye wanga mfumu, kapena mpa imfa kapena mpa moyo, pomwepo padzakhalanso mnyamata wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Itai nayankha mfumu nuti, Pali Yehova, pali mbuye wanga mfumu, zoonadi apo padzakhala mbuye wanga mfumu, kapena mpa imfa kapena mpa moyo, pomwepo padzakhalanso mnyamata wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Koma Itai adayankha mfumu kuti, “Pali Chauta wamoyo, ndiponso pali inu nomwe mbuyanga mfumu, kulikonse kumene inu mbuyanga mfumu mudzakhale, kaya mpa imfa kaya mpa moyo, ine mtumiki wanu ndidzakhalanso komweko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Koma Itai anayankha mfumu kuti, “Pali Yehova wamoyo, kulikonse kumene mbuye wanga mfumu mudzakhala, kaya ndi moyo kapena imfa, mtumiki wanu adzakhala komweko.” Onani mutuwo |