Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 14:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo mfumu inanena ndi mkaziyo, Pita kunyumba yako, ndipo ndidzalamulira za iwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo mfumu inanena ndi mkaziyo, Pita kunyumba yako, ndipo ndidzalamulira za iwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Apo mfumu idauza mkazi uja kuti, “Mai, pitani kunyumba kwanu, ndichitapo kanthu ineyo pa nkhaniyi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mfumu inati kwa mkaziyo, “Pitani ku nyumba kwanu ndipo ine ndidzalamula mʼmalo mwanu.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 14:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, chibale chonse chinaukira mdzakazi wanu, ndi kuti, Upereke iye amene anakantha mbale wake, kuti timuphe chifukwa cha moyo wa mbale wake amene anamupha; koma pakutero adzaononga wolowa yemwe; chomwecho adzazima khala langa lotsala, ndipo sadzasiyira mwamuna wanga dzina kapena mbeu kunja kuno.


Ndipo mkazi wa ku Tekowayo ananena ndi mfumu, Mbuye wanga mfumu, mphulupulu ikhale pa ine ndi pa nyumba ya atate wanga; ndipo mfumu ndi mpando wachifumu wao zikhale zopanda chifukwa.


Pomwepo mfumu inanena ndi Ziba, Ona, za Mefiboseti zonse zili zako. Ndipo Ziba anati, Ndikulambirani, mundikomere mtima, mbuye wanga mfumu.


Ndinali atate wa waumphawi; ndi mlandu wa iye amene sindinamdziwe ndinafunsitsa.


Wobwezera mau asanamvetse apusa, nadzichititsa manyazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa