2 Samueli 13:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Davide anatumiza mau kwao kwa Tamara, kuti, Upite kunyumba ya mlongo wako Aminoni, numkonzere chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Davide anatumiza mau kwao kwa Tamara, kuti, Upite kunyumba ya mlongo wako Aminoni, numkonzere chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Davide adatumiza mau kwa Tamara kuti, “Upite kunyumba kwa mbale wako Aminoni, ukamphikire chakudya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Davide anatumiza mawu kwa Tamara ku nyumba yaufumu kuti, “Pita ku nyumba ya mlongo wako Amnoni ndipo ukamukonzere chakudya.” Onani mutuwo |