2 Samueli 13:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo Yonadabu ananena ndi mfumu, Onani, ana aamuna a mfumu afika; monga ananena mnyamata wanu, momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo Yonadabu ananena ndi mfumu, Onani, ana amuna a mfumu afika; monga ananena mnyamata wanu, momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Atamva zimenezi Yonadabu adauza mfumu kuti, “Ana a mfumu abwera. Amfumu, monga momwe ndinakuuzirani muja, ndi m'mene zayendera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Yehonadabu anati kwa mfumu, “Taonani ana a mfumu afika. Zachitika monga momwe mtumiki wanu ananenera.” Onani mutuwo |