Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 13:33 - Buku Lopatulika

33 Chifukwa chake tsono mfumu mbuye wanga asasauke mtima ndi chinthuchi, ndi kuganiza kuti ana aamuna onse a mfumu afa; pakuti Aminoni yekha wafa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Chifukwa chake tsono mfumu mbuye wanga asasauke mtima ndi chinthuchi, ndi kuganiza kuti ana amuna onse a mfumu afa; pakuti Aminoni yekha wafa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Nchifukwa chake tsono mbuyanga mfumu, musavutike ndi maganizo oti ana anu onse aamuna aphedwa. Aminoni yekha ndiye waphedwa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Mbuye wanga mfumu musavutike ndi maganizo ndi nkhani yoti ana onse a mfumu afa. Wafa ndi Amnoni yekha.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 13:33
2 Mawu Ofanana  

Koma Abisalomu anathawa. Ndipo mnyamata wakudikira anatukula maso ake nayang'ana, ndipo onani, m'mbuyo mwake anthu ambiri analikubwera m'njira yolambalala phiri.


Nati kwa mfumu, Mbuye wanga asandiwerengere ine mphulupulu ndiponso musakumbukire chimene mnyamata wanu ndinachita mwamphulupulu tsiku lija mbuye wanga mfumu anatuluka ku Yerusalemu, ngakhale kuchisunga mumtima mfumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa