2 Samueli 13:21 - Buku Lopatulika21 Koma pamene mfumu Davide anamva zonsezi, anakwiya ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma pamene mfumu Davide anamva zonsezi, anakwiya ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Davide atazimva zimenezi, adapsa nazo mtima zedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mfumu Davide itamva zimenezi, inakwiya kwambiri. Onani mutuwo |