Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 11:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo Davide anatumiza munthu nafunsa za mkaziyo. Ndipo wina anati, Sindiye Bateseba, mwana wamkazi wa Eliyamu, mkazi wa Uriya Muhiti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo Davide anatumiza munthu nafunsa za mkaziyo. Ndipo wina anati, Sindiye Bateseba, mwana wamkazi wa Eliyamu, mkazi wa Uriya Muhiti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pomwepo Davide adatuma munthu kuti akafunsitse za mkaziyo. Ndipo munthuyo adamuuza kuti, “Mkazi ujatu ndi Bateseba, mwana wa Eliyamu, mwamuna wake ndi Uriya Muhiti.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndipo Davide anatuma munthu wina kuti akafufuze za iye. Munthuyo anati, “Kodi uyu si Batiseba, mwana wa Eliamu, mkazi wa Uriya Mhiti?”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 11:3
10 Mawu Ofanana  

koma wosaukayo analibe kanthu kena koma kamwana kakakazi ka nkhosa, kamene anakagula ndi kukaweta; ndipo kameneko kanakula naye pamodzi ndi ana ake. Kanadyako chakudya chake cha iye yekha, kanamwera m'chikho cha iye yekha, kanagona pa chifukato chake, ndipo kanali kwa iye ngati mwana wake wamkazi.


Elifeleti mwana wa Ahasibai, mwana wa Mmaaka, Eliyamu mwana wa Ahitofele Mgiloni;


Uriya Muhiti; onse pamodzi anali makumi atatu mphambu asanu ndi awiri.


chifukwa kuti Davide adachita cholungama pamaso pa Yehova, osapatuka masiku ake onse pa zinthu zonse adamlamulira Iye, koma chokhacho chija cha Uriya Muhiti.


Uriya Muhiti, Zabadi mwana wa Alai,


Ndipo ombadwira mu Yerusalemu ndi awa: Simea, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomoni, anai a Batisuwa mwana wamkazi wa Amiyele;


Asakuchititse kaso m'mtima mwako, asakukole ndi zikope zake.


Anali onga akavalo okhuta mamawa; yense wakumemesera mkazi wa mnansi wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa