Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 11:20 - Buku Lopatulika

20 kudzali kuti ukapsa mtima wa mfumu nikati kwa iwe, Chifukwa ninji munayandikira pafupi potere pamzinda kukamenyana nao? Simunadziwe kodi kuti apalingawo adzaponya?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 kudzali kuti ukapsa mtima wa mfumu nikati kwa iwe, Chifukwa ninji munayandikira pafupi potere pamudzi kukamenyana nao? Simunadziwa kodi kuti apalingawo adzaponya?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 tsono ngati mfumu ikapse mtima, nikakufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani mudapita kufupi ndi mzinda kuti mukamenye nkhondo? Kodi simunkadziŵa kuti adzakulasani kuchokera m'kati mwa linga?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 mfumu ikapsa mtima, ndipo akakakufunsa kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani munapita pafupi ndi mzindawo kukamenya nkhondo? Inu simunadziwe kuti atha kukuponyerani mivi kuchokera pa khoma?

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 11:20
2 Mawu Ofanana  

nauza mthengawo kuti, Utatsiriza kuuza mfumu zonse za nkhondozo;


Ndani anakantha Abimeleki mwana wa Yerubeseti? Sadamponyera kodi mphero mkazi wa palinga nafa iye ku Tebezi? Munasendera bwanji pafupi potere pa lingalo? Tsono udzanena, Mnyamata wanu Uriya Muhiti, iyenso adafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa