2 Samueli 10:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo pamene Davide anachimva, anatumiza Yowabu ndi khamu lonse la anthu amphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo pamene Davide anachimva, anatumiza Yowabu ndi khamu lonse la anthu amphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Davide atamva zimenezo, adatuma Yowabu ndi gulu lake lonse la ankhondo, amphamvu okhaokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Davide atamva zimenezi, anatumiza Yowabu ndi gulu lonse la ankhondo amphamvu. Onani mutuwo |