2 Samueli 10:10 - Buku Lopatulika10 Koma anthu otsalawo anawapereka kwa Abisai mbale wake, amene anawandandalitsa cha kwa Amoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma anthu otsalawo anawapereka kwa Abisai mbale wake, amene anawandandalitsa cha kwa Amoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Anthu ena onse otsala adaŵaika m'manja mwa Abisai, mbale wake, ndipo adaŵandanditsa moyang'anana ndi Aamoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iye anayika ankhondo ena otsalawo mʼmanja mwa Abisai mʼbale wake ndipo anawayika kuti amenyane ndi Aamoni. Onani mutuwo |