2 Samueli 1:20 - Buku Lopatulika20 Usachinene ku Gati, usachibukitse m'makwalala a Asikeloni, kuti ana aakazi a Afilisti angasekere, kuti ana aakazi a osadulidwawo angafuule mokondwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Usachinene ku Gati, usachibukitse m'makwalala a Asikeloni, kuti ana akazi a Afilisti angasekere, kuti ana akazi a osadulidwawo angafuule mokondwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Musakanene zimenezi ku Gati, musakalengeze m'miseu ya ku Asikeloni, kuti akazi a Afilisti angasekerere, akazi a anthu osaumbalidwa angakondwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Musakanene zimenezi ku Gati, musazilengeze ku misewu ya ku Asikeloni, kuti ana aakazi a Afilisti angasangalale, ana aakazi a osachita mdulidwe angakondwere. Onani mutuwo |