2 Mbiri 4:9 - Buku Lopatulika9 Anamanganso bwalo la ansembe, ndi bwalo lalikulu, ndi zitseko za kubwalo, nakuta zitseko zake ndi mkuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anamanganso bwalo la ansembe, ndi bwalo lalikulu, ndi zitseko za kubwalo, nakuta zitseko zake ndi mkuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Adapanga bwalo la ansembe, bwalo lalikulu, ndiponso zitseko za bwalo, nazikuta ndi mkuŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye anapanga bwalo la ansembe, bwalo lalikulu ndi zitseko za bwalolo ndipo anakuta zitsekozo ndi mkuwa. Onani mutuwo |