Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 4:9 - Buku Lopatulika

9 Anamanganso bwalo la ansembe, ndi bwalo lalikulu, ndi zitseko za kubwalo, nakuta zitseko zake ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Anamanganso bwalo la ansembe, ndi bwalo lalikulu, ndi zitseko za kubwalo, nakuta zitseko zake ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Adapanga bwalo la ansembe, bwalo lalikulu, ndiponso zitseko za bwalo, nazikuta ndi mkuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iye anapanga bwalo la ansembe, bwalo lalikulu ndi zitseko za bwalolo ndipo anakuta zitsekozo ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 4:9
6 Mawu Ofanana  

Ndipo bwalo la m'kati analimanga mizere itatu ya miyala yosemasema, ndi mzere umodzi wa mitanda yamkungudza.


Ndipo bwalo lalikulu lozingapo linali ndi mizere itatu ya miyala yosemasema, ndi mzere umodzi wa mitanda yamkungudza, monga bwalo la pakati pa nyumba ya Yehova, ndi chipinda cholowera cha nyumbayo.


Nalimangira khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehova.


Namangiranso khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehova.


Upangenso bwalo la chihema; pa mbali yake ya kumwera, kumwera, pakhale nsalu zotchingira za kubwalo za nsalu yabafuta wa thonje losansitsa, utali wake wa pa mbali imodzi mikono zana;


Atatha tsono kuyesa nyumba ya m'katimo, anatuluka nane njira ya chipata choloza kum'mawa nayesa bwalo pozungulira pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa