2 Mbiri 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anaika thawalelo ku dzanja lamanja la nyumba kum'mawa chakumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anaika thawalelo ku dzanja lamanja la nyumba kum'mawa chakumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo adaika thanki lija pa ndonyo yakumwera ya Nyumbayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anayika mbiya ija mbali yakummwera pamene mbali ya kummawa ndi kummwera zimakumana. Onani mutuwo |