2 Mbiri 4:2 - Buku Lopatulika2 Anayenganso thawale losungunula la mikono khumi kukamwa, lozunguniza, ndi msinkhu wake mikono isanu; ndi chingwe cha mikono makumi atatu chinalizunguniza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Anayenganso thawale losungunula la mikono khumi kukamwa, lozunguniza, ndi msinkhu wake mikono isanu; ndi chingwe cha mikono makumi atatu chinalizunguniza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pambuyo pake adapanga thanki. Thankilo linali loulungika. Pakamwa pake panali pa mamita anai ndi theka, kuyesa modutsa pakati pake. Msinkhu wake unali wa mamita aŵiri nkanthu, ndipo kuzungulira m'thunthu mwake munali mamita 13 ndi theka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kenaka iye anapanga mbiya yayikulu yachitsulo. Inali yozungulira ndipo pakamwa pake panali pa mamita anayi ndi theka, poyeza modutsa pakati pake. Msinkhu wake unali wopitirirapo mamita awiri. Thunthu lake linali mamita 13. Onani mutuwo |