2 Mbiri 1:4 - Buku Lopatulika4 Koma likasa la Mulungu Davide adakwera nalo kuchokera ku Kiriyati-Yearimu kunka kumene Davide adalikonzeratu malo; pakuti adaliutsiratu hema ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma likasa la Mulungu Davide adakwera nalo kuchokera ku Kiriyati-Yearimu kunka kumene Davide adalikonzeratu malo; pakuti adaliutsiratu hema ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 (Davide anali atabwera nalo bokosi lachipangano la Chauta kuchokera ku Kiriyati-Yearimu, ndi kulikhazika ku malo amene iye adaakonza, poti adaalimangira hema ku Yerusalemu.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Davide anabweretsa Bokosi la Mulungu kuchokera ku Kiriyati Yearimu, ndi kulikhazika kumalo kumene analikonzera popeza analimangira tenti mu Yerusalemu. Onani mutuwo |