2 Mafumu 2:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kunali ataoloka, Eliya anati kwa Elisa, Tapempha chimene ndikuchitire ndisanachotsedwe kwa iwe. Ndipo Elisa anati, Mundipatse magawo awiri a mzimu wanu akhale pa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kunali ataoloka, Eliya anati kwa Elisa, Tapempha chimene ndikuchitire ndisanachotsedwe kwa iwe. Ndipo Elisa anati, Mundipatse magawo awiri a mzimu wanu akhale pa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ataoloka, Eliya adauza Elisa kuti, “Undipemphe choti ndikuchitire ndisanakusiye.” Elisa adati, “Ndikukupemphani kuti ndilandire chigawo chachikulu cha mphamvu zanu za uneneri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Atawoloka, Eliya anati kwa Elisa, “Ndifotokozere, ndikuchitire chiyani ndisanachotsedwe pamaso pako?” Elisa anayankha kuti, “Ndikupemphani kuti mundipatse magawo awiri a mphamvu za mzimu wanu wa uneneri.” Onani mutuwo |