2 Akorinto 8:24 - Buku Lopatulika24 Chifukwa chake muwatsimikizire iwo chitsimikizo cha chikondi chanu, ndi cha kudzitamandira kwathu pa inu pamaso pa Mipingo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Chifukwa chake muwatsimikizire iwo chitsimikizo cha chikondi chanu, ndi cha kudzitamandira kwathu pa inu pamaso pa Mipingo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono muŵatsimikizire chikondi chanu, kuti mipingo yonse ichiwone, ndi kudziŵa kuti sitikulakwa tikamakunyadirani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Choncho anthu amenewa atsimikizireni za chikondi chanu ndipo adziwe chifukwa chimene ife timakunyadirani, kuti mipingo yonse iwone chimenechi. Onani mutuwo |