Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 7:16 - Buku Lopatulika

16 Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ndikukondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ndine wokondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 7:16
5 Mawu Ofanana  

nulimbika mumtima kuti iwe wekha uli wotsogolera wa akhungu, nyali ya amene akhala mumdima,


Ndipo ndinalemba ichi chomwe, kuti pakudza ndisakhale nacho chisoni kwa iwo amene ayenera kukondweretsa ine; ndi kukhulupirira mwa inu nonse, kuti chimwemwe changa ndi chanu cha inu nonse.


koma tikhulupirira mwa Ambuye za inu, kuti mumachita, ndiponso mudzachita zimene tikulamulirani.


Pokhulupirira kumvera kwako ndikulembera iwe, podziwa kuti udzachitanso koposa chimene ndinena.


Momwemo, ndingakhale ndili nako kulimbika mtima kwakukulu mu Khristu kukulamulira chimene chiyenera,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa