2 Akorinto 4:8 - Buku Lopatulika8 ndife osautsika monsemo, koma osapsinjika; osinkhasinkha, koma osakhala kakasi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndife osautsika monsemo, koma osapsinjika; osinkhasinkha, koma osakhala kakasi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tikuwona masautso a mtundu uliwonse, koma osapsinjidwa. Tikuthedwa nzeru, koma osataya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tapanikizika kwambiri mbali zonse koma osaphwanyika; tathedwa nzeru koma osataya mtima; Onani mutuwo |
Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Wandivutiranji kundikweretsa kuno? Saulo nayankha, Ndilikusautsika kwambiri, pakuti Afilisti aponyana nkhondo ndi ine, ndipo Mulungu anandichokera, osandiyankhanso, kapena ndi aneneri, kapena ndi maloto; chifukwa chake ndakuitanani, kuti mundidziwitse chimene ndiyenera kuchita.