2 Akorinto 4:7 - Buku Lopatulika7 Koma tili nacho chuma ichi m'zotengera zadothi, kuti ukulu woposa wamphamvu ukhale wa Mulungu, wosachokera kwa ife; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma tili nacho chuma ichi m'zotengera zadothi, kuti ukulu woposa wamphamvu ukhale wa Mulungu, wosachokera kwa ife; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma ife ndife mbiya zadothi chabe zosungiramo chumachi, kuti padziŵike kuti mphamvu zazikulu zoterezi ndi za Mulungu, osati zathu ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma tili ndi chuma ichi mʼmbiya zadothi, kusonyeza kuti mphamvu yoposayi, imachokera kwa Mulungu osati kwa ife. Onani mutuwo |