2 Akorinto 3:8 - Buku Lopatulika8 koposa kotani nanga utumiki wa Mzimu udzakhala mu ulemerero? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 koposa kotani nanga utumiki wa Mzimu udzakhala m'ulemerero? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 nanji ntchito ya Mzimu Woyera, kodi siidzakhala ndi ulemerero wopambana pamenepo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 kodi nanga utumiki wa Mzimu sudzaposa apa? Onani mutuwo |