2 Akorinto 3:17 - Buku Lopatulika17 Koma Ambuye ndiye Mzimuyo; ndipo pamene pali Mzimu wa Ambuye pali ufulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma Ambuye ndiye Mzimuyo; ndipo pamene pali Mzimu wa Ambuye pali ufulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono tikamati, “Ambuye,” tikunena Mzimu Woyera. Ndipo kumene kuli Mzimu wa Ambuye, kuli ufulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tsono Ambuye ndi Mzimu, ndipo pamene pali Mzimu wa Ambuye, pali ufulu. Onani mutuwo |