2 Akorinto 2:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti chifukwa cha ichi ndalembanso, kuti ndidziwe mayesedwe anu, ngati muli omvera m'zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti chifukwa cha ichi ndalembanso, kuti ndidziwe mayesedwe anu, ngati muli omvera m'zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pamene ndinkakulemberani kalata ija, cholinga changa chinali chakuti ndikuyeseni, ndi kuwona ngati mudzandimvera pa zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Cholinga china chimene ndinakulemberani kalata ija chinali chofuna kukuonani ngati mudzandimvera pa zonse. Onani mutuwo |