2 Akorinto 2:13 - Buku Lopatulika13 ndinalibe mpumulo mu mzimu wanga, posapeza ine Tito mbale wanga; koma polawirana nao ndinanka ku Masedoniya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndinalibe mpumulo mu mzimu wanga, posapeza ine Tito mbale wanga; koma polawirana nao ndinanka ku Masedoniya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Komabe mumtima mwanga munalibe mtendere, chifukwa sindidampeze Tito, mbale wanga. Tsono ndidatsazikana ndi anthu akumeneko nkupita ku Masedoniya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 ndinasowa mtendere mu mtima mwanga, chifukwa sindinapezeko mʼbale wanga Tito. Choncho ndinatsanzikana ndi anthu kumeneko nʼkupita ku Makedoniya. Onani mutuwo |