2 Akorinto 2:1 - Buku Lopatulika1 Koma ndinatsimikiza mtima mwa ine ndekha, ndisadzenso kwa inu ndi chisoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma ndinatsimikiza mtima mwa ine ndekha, ndisadzenso kwa inu ndi chisoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nchifukwa chake ndidatsimikiza kuti ndisachite ulendo winanso wopweteka wobwera kwanuko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kotero ndinatsimikiza maganizo anga kuti ndisachitenso ulendo wina owawa wobwera kwanuko. Onani mutuwo |