2 Akorinto 13:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti tikondwera, pamene ife tifooka ndi inu muli amphamvu; ichinso tipempherera, ndicho ungwiro wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti tikondwera, pamene ife tifooka ndi inu muli amphamvu; ichinso tipempherera, ndicho ungwiro wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Timakondwa pamene ife tili ofooka koma inu muli amphamvu. Chimene tikupempha Mulungu nchakuti mudzasanduke angwiro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ife timasangalala kuti pamene tafowoka, inu muli amphamvu; ndipo pemphero lathu ndi lakuti mukhale angwiro. Onani mutuwo |