Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 12:5 - Buku Lopatulika

5 Chifukwa cha wotereyo ndidzadzitamandira; koma chifukwa cha ine ndekha sindidzadzitamandira, koma m'zofooka zanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Chifukwa cha wotereyo ndidzadzitamandira; koma chifukwa cha ine ndekha sindidzadzitamandira, koma m'zofooka zanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Munthu wotere ndidzamnyadira, koma kunena za ine ndekha, sindidzanyadira kanthu kena koma kufooka kwanga kokha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndidzatamanda za munthu ngati ameneyu, koma sindidzadzitamandira ine mwini kupatula za kufowoka kwanga.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 12:5
5 Mawu Ofanana  

kotero kuti chikwaniridwe chonenedwa ndi Yesaya mneneri, kuti, Iye yekha anatenga zofooka zathu, nanyamula nthenda zathu.


Ndipo ine ndinakhala nanu mofooka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri.


Ngati ndiyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira ndi za kufooka kwanga.


Ndiyenera kudzitamandira, kungakhale sikupindulika; koma ndidzadza kumasomphenya ndi mavumbulutso a Ambuye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa