2 Akorinto 11:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti otere ali atumwi onyenga, ochita ochenjerera, odzionetsa ngati atumwi a Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti otere ali atumwi onyenga, ochita ochenjerera, odzionetsa ngati atumwi a Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Anthu otereŵa si atumwi oona, koma antchito onyenga, amene amadzizimbaitsa, naoneka ngati atumwi a Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti anthu oterewa ndi atumwi onama, antchito achinyengo, odzizimbayitsa ngati atumwi a Khristu. Onani mutuwo |