2 Akorinto 10:9 - Buku Lopatulika9 kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa makalatawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa akalatawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono musayese kuti ndikungokuwopsezani ndi makalata anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ine sindikufuna kuoneka ngati ndikukuopsezani ndi makalata anga. Onani mutuwo |