Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 10:9 - Buku Lopatulika

9 kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa makalatawo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa akalatawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsono musayese kuti ndikungokuwopsezani ndi makalata anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ine sindikufuna kuoneka ngati ndikukuopsezani ndi makalata anga.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 10:9
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake musaweruze kanthu isanadze nthawi yake, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wake wa kwa Mulungu.


Pakuti, makalatatu, ati, ndiwo olemera, ndi amphamvu; koma maonekedwe a thupi lake ngofooka, ndi mau ake ngachabe.


Pakuti ndingakhale ndikadzitamandira kanthu kochulukira za ulamuliro (umene anatipatsa Ambuye kukumangirira, ndipo si kukugwetsera kwanu), sindidzanyazitsidwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa