2 Akorinto 10:4 - Buku Lopatulika4 (pakuti zida za nkhondo yathu sizili za thupi, koma zamphamvu mwa Mulungu zakupasula malinga); Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 (pakuti zida za nkhondo yathu sizili za thupi, koma zamphamvu mwa Mulungu zakupasula malinga); Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pakuti zida zathu zakhondo si za anthu chabe, koma ndi mphamvu zochokera kwa Mulungu zotha kuwononga malinga. Timagonjetsa maganizo onyenga, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti zida zathu zankhondo si zida za dziko lapansi. Koma ndi mphamvu zochokera kwa Mulungu zotha kugwetsa malinga. Onani mutuwo |