1 Yohane 3:7 - Buku Lopatulika7 Tiana, munthu asasokeretse inu; iye wakuchita cholungama ali wolungama, monga Iyeyu ali wolungama: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tiana, munthu asasokeretse inu; iye wakuchita cholungama ali wolungama, monga Iyeyu ali wolungama: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ana anga, wina aliyense asakusokeretseni. Munthu amene amachita chilungamo, ngwolungama monga Khristu ali wolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ana okondedwa, musalole kuti aliyense akusocheretseni. Munthu amene amachita chilungamo ndi wolungama, monga Khristu ali wolungama. Onani mutuwo |