1 Yohane 2:7 - Buku Lopatulika7 Okondedwa, sindikulemberani lamulo latsopano, komatu lamulo lakale limene munali nalo kuyambira pa chiyambi; lamulo lakalelo ndilo mau amene mudawamva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Okondedwa, sindikulemberani lamulo latsopano, komatu lamulo lakale limene munali nalo kuyambira pa chiyambi; lamulo lakalelo ndilo mau amene mudawamva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu okondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano, koma lakale lomwe lija, limene mwakhala nalo kuyambira pa chiyambi. Lamulo lakalelo ndi mau amene mudaŵamva kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Okondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano koma lakale lomwe lija, limene munali nalo kuyambira pachiyambi. Lamulo la kalelo ndi mawu amene munawamva kale. Onani mutuwo |