1 Yohane 2:4 - Buku Lopatulika4 Iye wakunena kuti, Ndimdziwa Iye, koma wosasunga malamulo ake, ali wabodza, ndipo mwa iye mulibe choonadi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Iye wakunena kuti, Ndimdziwa Iye, koma wosasunga malamulo ake, ali wabodza, ndipo mwa iye mulibe choonadi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Munthu akamati, “Ine ndimadziŵa Mulungu”, koma chikhalirecho satsata malamulo ake, angonama ameneyo, ndipo mwa iye mulibe choona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Munthu akamanena kuti, “Ine ndimadziwa Mulungu,” koma samvera malamulo a Mulunguyo, ndi wabodza ameneyo ndipo mwa iye mulibe choonadi. Onani mutuwo |