1 Yohane 2:2 - Buku Lopatulika2 ndipo Iye ndiye chiombolo cha machimo athu; koma wosati athu okha, komanso a dziko lonse lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo Iye ndiye chiombolo cha machimo athu; koma wosati athu okha, komanso a dziko lonse lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyeyo ndiye nsembe yopepesera machimo athu, ndipo osati athu okha, komanso a anthu a pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iyeyo ndiye nsembe yopepesera machimo athu, ndipo osati athu okha, komanso machimo onse a dziko lapansi. Onani mutuwo |