1 Timoteyo 5:3 - Buku Lopatulika3 Chitira ulemu amasiye amene ali amasiye ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chitira ulemu amasiye amene ali amasiye ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Uziŵachitira ulemu azimai amasiye, amenetu ali amasiye enieni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Uziwachitira ulemu akazi amasiye amene ali okhaokha. Onani mutuwo |
Ndipo mukondwere pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu ndi ana anu aamuna, ndi ana anu aakazi, ndi antchito anu aamuna, ndi antchito anu aakazi, ndi Mlevi wokhala m'mudzi mwanu, ndi mlendo, ndi mwana wamasiye, ndi mkazi wamasiye, okhala pakati pa inu, m'malo amene Yehova Mulungu wanu adzasankha kukhalitsako dzina lake.