1 Timoteyo 5:2 - Buku Lopatulika2 akazi aakulu ngati amai; akazi aang'ono ngati alongo, m'kuyera mtima konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 akazi akulu ngati amai; akazi aang'ono ngati alongo, m'kuyera mtima konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Azimai achikulire uzikhalitsana nawo ngati amai ako, ndipo azimai a zaka zochepa uzikhalitsana nawo ngati alongo ako, m'kuyera mtima kwenikweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Amayi achikulire uwatenge ngati amayi ako ndipo amayi achitsikana uwatenge ngati alongo ako, nʼkuyera mtima konse. Onani mutuwo |