1 Timoteyo 4:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti cholengedwa chonse cha Mulungu nchabwino, ndipo palibe kanthu kayenera kutayika, ngati kalandiridwa ndi chiyamiko; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti cholengedwa chonse cha Mulungu nchabwino, ndipo palibe kanthu kayenera kutayika, ngati kalandiridwa ndi chiyamiko; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pajatu chilichonse chimene Mulungu adalenga nchabwino, palibe chilichonse choti munthu asale, akamachilandira moyamika Mulungu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti chilichonse chimene Mulungu analenga ndi chabwino, ndipo chilichonse chisasalidwe, akamachilandira moyamika, Onani mutuwo |