Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 4:5 - Buku Lopatulika

5 pakuti kayeretsedwa ndi Mau a Mulungu ndi kupemphera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 pakuti kayeretsedwa ndi Mau a Mulungu ndi kupemphera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 pakuti chimayeretsedwa ndi mau a Mulungu ndi mapemphero aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 pakuti chimayeretsedwa ndi mawu a Mulungu ndi pemphero.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 4:5
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anapanga zinyama za dziko lapansi monga mwa mitundu yao; ndi ng'ombe monga mwa mtundu wake, ndi zonse zokwawa pansi monga mwa mitundu yao; ndipo Mulungu anaona kuti kunali kwabwino.


Ndipo anaziona Mulungu zonse zimene adazipanga, ndipo, taonani, zinali zabwino ndithu. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu ndi chimodzi.


Koma patsani mphatso yachifundo za m'katimo; ndipo onani, zonse zili zoyera kwa inu.


Ndipo Yesu anayankha nati kwa iye, Kwalembedwa, kuti, Munthu sadzakhala ndi moyo ndi mkate wokha.


Pakuti mwamuna wosakhulupirirayo ayeretsedwa mwa mkaziyo, ndi mkazi wosakhulupirira ayeretsedwa mwa mbaleyo; ngati sikukadatero, ana anu akadakhala osakonzeka, koma tsopano akhala oyera.


a kuletsa ukwati, osiyitsa zakudya zakuti, zimene Mulungu anazilenga kuti achikhulupiriro ndi ozindikira choonadi azilandire ndi chiyamiko.


Zonse ziyera kwa iwo amene ayera mtima; koma kwa iwo odetsedwa ndi osakhulupirira kulibe kanthu koyera; komatu zadetsedwa nzeru zao ndi chikumbumtima chao.


Ndi chikhulupiriro tizindikira kuti maiko ndi a m'mwamba omwe anakonzedwa ndi mau a Mulungu, kotero kuti zinthu zopenyeka sizinapangidwe kuchokera mu zoonekazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa