1 Samueli 9:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo pamene analikutsika polekeza mzinda, Samuele ananena ndi Saulo, Uzani mnyamatayo abatsogola; napita iyeyo. Koma inu muime pano, kuti ndikumvetseni mau a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo pamene analikutsika polekeza mudzi, Samuele ananena ndi Saulo, Uzani mnyamatayo abatsogola; napita iyeyo. Koma inu muime pano, kuti ndikumvetseni mau a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Atafika kothera kwake kwa mzindawo, Samuele adauza Saulo kuti, “Uza mnyamatayu kuti abatsogola, iwe wekha uime pang'ono, kuti ndikuuze mau ochokera kwa Mulungu.” Mnyamata uja adatsogola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atakafika ku mathero a mzindawo, Samueli anati kwa Sauli, “Muwuzeni mnyamata wanu kuti atsogole, koma inuyo muyime pangʼono kuti ndikuwuzeni mawu ochokera kwa Mulungu.” Onani mutuwo |