Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 9:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo Samuele anatenga Saulo ndi mnyamata wake, napita nao ku chipinda cha alendo, nawakhalitsa pamalo a ulemu pakati pa oitanidwa onse; ndiwo anthu monga makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo Samuele anatenga Saulo ndi mnyamata wake, napita nao ku chipinda cha alendo, nawakhalitsa pa malo a ulemu pakati pa oitanidwa onse; ndiwo anthu monga makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Tsono Samuele adatenga Saulo ndi mnyamata wake uja, ndipo adaloŵa nawo m'chipinda chachikulu, naŵapatsa malo kutsogolo kwa anthu oitanidwa, amene onse pamodzi anali ngati anthu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ndipo Samueli anatenga Sauli ndi mnyamata wake uja ndi kulowa nawo mʼchipinda chachikulu ndipo anawakhazika kutsogolo kwa anthu oyitanidwa. Onse pamodzi analipo anthu makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 9:22
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuikira iye chake pa yekha, ndi iwo chao pa okha, ndi Aejipito akudya naye chao pa okha; chifukwa Aejipito sanathei kudya chakudya pamodzi ndi Ahebri: chifukwa kuchita chomwecho nkunyansira Aejipito.


Koma pamene paliponse waitanidwa iwe, pita nukhale pansi pa malo a kuthungo; kotero kuti pamene akadza iye anakuitana iwe, akanena ndi iwe, Bwenzi langa, sendera, kwera kuno; pomwepo udzakhala ndi ulemerero pamaso pa onse akuseama pachakudya pamodzi ndi iwe.


Ndipo Saulo anayankha nati, Sindili Mbenjamini kodi wa fuko laling'ono mwa Israele? Ndiponso banja lathu nlochepa pakati pa mabanja onse a fuko la Benjamini? Potero mulankhula bwanji mau otere ndi ine?


Ndipo Samuele ananena ndi wophika, Tenga nyama ndinakupatsa, ndi kuti, Ibakhala ndi iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa