1 Samueli 7:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anabwera ku Rama, pakuti nyumba yake inali kumeneko; ndipo pamenepo anaweruza Israele; namangapo guwa la nsembe la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anabwera ku Rama, pakuti nyumba yake inali kumeneko; ndipo pamenepo anaweruza Israele; namangapo guwa la nsembe la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pambuyo pake ankabwerera ku Rama, poti ndiko kunali kwao. Kumenekonso ankaweruza Aisraele, ndipo adamangirako Chauta guwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma pambuyo pake ankabwerera ku Rama, kumene kunali nyumba yake. Ankaweruza Aisraeli kumeneko. Ndipo iye anamanga guwa lansembe la Yehova kumeneko. Onani mutuwo |