1 Samueli 30:14 - Buku Lopatulika14 Tinathira nkhondo kumwera kwa Akereti ndi ku dziko lija la Ayuda, ndi kumwera kwa Kalebe; ndipo tinatentha mudzi wa Zikilagi ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Tinathira nkhondo kumwera kwa Akereti ndi ku dziko lija la Ayuda, ndi kumwera kwa Kalebe; ndipo tinatentha mudzi wa Zikilagi ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tinkathira nkhondo dera la kumwera kwa Yuda, ku maiko a Akereti, ndi dera la Akalebe. Mwakuti tidatentha mzinda wa Zikilagi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ife tinathira nkhondo dera la kummwera kwa mayiko a Akereti, dera la Yuda, ndi dera la kummwera kwa mayiko a Kalebe. Mzinda wa Zikilagi tinawutentha ndi moto.” Onani mutuwo |