Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 3:7 - Buku Lopatulika

7 Koma Samuele sanadziwe Yehova, ndiponso mau a Yehova sanaululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma Samuele sanadziwe Yehova, ndiponso mau a Yehova sanaululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pamenepo nkuti Samuele asanadziŵe Chauta, ndipo mau a Chauta nkuti asanaululidwe kwa iyeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Nthawiyi nʼkuti Samueli asanadziwe Yehova ndipo Mawu a Yehova nʼkuti asanawululidwe kwa iye.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 3:7
5 Mawu Ofanana  

koma wakudzitamandira adzitamandire adzikweze umo, kuti ali wakuzindikira, ndi kundidziwa Ine, kuti ndine Yehova wakuchita zokoma mtima, chiweruziro, ndi chilungamo m'dziko lapansi, pakuti m'menemo ndikondwerera, ati Yehova.


ndipo anati kwa iwo, Kodi munalandira Mzimu Woyera pamene munakhulupirira? Ndipo anati, Iai, sitinamve konse kuti Mzimu Woyera waperekedwa.


Pamene ndinali mwana, ndinalankhula ngati mwana, ndinalingirira ngati mwana, ndinawerenga ngati mwana; tsopano ndakhala munthu, ndayesa chabe zachibwana.


Ndipo Yehova anabwereza kumuitana, ndi kuti, Samuele. Ndipo Samuele anauka, napita kwa Eli, nati, Ndine, pakuti mwandiitana ndithu. Koma iye anayankha, Sindinaitane, mwana wanga; kagone.


Ndipo Yehova anabwereza kumuitana Samuele nthawi yachitatu. Ndipo iye anauka napita kwa Eli, nati, Ndine, pakuti mwandiitana ndithu. Ndipo Eli anazindikira kuti ndiye Yehova amene analikuitana mwanayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa